2 Mafumu 13:11 - Buku Lopatulika11 Nachita choipa pamaso pa Yehova, osazileka zolakwa zonse za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele, koma anayendamo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nachita choipa pamaso pa Yehova, osazileka zolakwa zonse za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele, koma anayendamo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Nayenso adachita zoipa kuchimwira Chauta. Sadaleke kuchita zoipa zonse zimene ankachita Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene adachimwitsa nazo Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova ndipo sanaleke kuchita tchimo la Yeroboamu mwana wa Nebati limene anachimwitsa nalo Israeli. Onani mutuwo |