2 Mafumu 12:8 - Buku Lopatulika8 Navomera ansembe kusalandiranso ndalama za anthu, kapena kukonza mogamuka nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Navomera ansembe kusalandiranso ndalama za anthu, kapena kukonza mogamuka nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Motero ansembe aja adavomera kuti sadzatenganso ndalama kwa anthu, ndipo kuti sindiwo adzakonza Nyumbayo, koma ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ansembe anavomera kuti salandiranso ndalama kuchokera kwa anthu ndipo kuti sindiwo amene ati akonzenso nyumbayo. Onani mutuwo |