2 Mafumu 12:7 - Buku Lopatulika7 Pamenepo mfumu Yowasi anaitana Yehoyada wansembe, ndi ansembe ena, nanena nao, Mulekeranji kukonza mogamuka nyumba? Tsono musalandiranso ndalama kwa anzanu odziwana nao, kuziperekera mogamuka nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamenepo mfumu Yowasi anaitana Yehoyada wansembe, ndi ansembe ena, nanena nao, Mulekeranji kukonza mogamuka nyumba? Tsono musalandiranso ndalama kwa anzanu odziwana nao, kuziperekera mogamuka nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake mfumu Yowasi adaitana wansembe Yehoyada ndi ansembe ena, naŵafunsa kuti, “Chifukwa chiyani simukukonza Nyumbayi? Kuyambira tsopano, musasungenso ndalama za anthu amene mumaŵatumikira, koma muzipereke kuti akonzere Nyumbayi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Choncho Mfumu Yowasi inayitanitsa wansembe Yehoyada ndi ansembe ena ndipo inafunsa kuti, “Chifukwa chiyani simukukonza malo owonongeka a mʼnyumbayi? Musasungenso ndalama zina zochokera kwa abwenzi anu, koma muzipereke kuti akonzere nyumbayi.” Onani mutuwo |