2 Mafumu 12:6 - Buku Lopatulika6 Koma kunali, chaka cha makumi awiri mphambu zitatu cha mfumu Yowasi, ansembe sanathe kukonza mogamuka nyumba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma kunali, chaka cha makumi awiri mphambu zitatu cha mfumu Yowasi, ansembe sanathe kukonza mogamuka nyumba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Koma pomafika chaka cha 23 cha ufumu wa Yowasi, ansembewo anali asanakonzebe Nyumbayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Koma pofika chaka cha 23 cha ufumu wa Yowasi, ansembewo anali asanakonze nyumbayo. Onani mutuwo |