2 Mafumu 12:5 - Buku Lopatulika5 Ansembe azilandire yense kwa iye amene adziwana naye, akonze nazo mogamuka nyumba, paliponse akapeza pogamuka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ansembe azilandire yense kwa iye amene adziwana naye, akonze nazo mogamuka nyumba, paliponse akapeza pogamuka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Wansembe aliyense aziyang'anira ndalama zopereka anthu amene iye amaŵatumikira, ndipo azigwiritse ntchito pokonza Nyumba paliponse pamene pafunika kukonza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Wansembe aliyense alandire ndalamazo kuchokera kwa abwenzi ake, ndipo zigwiritsidwe ntchito yokonzera chilichonse chimene chipezeke kuti ndi chowonongeka mʼnyumbayo.” Onani mutuwo |