2 Mafumu 12:12 - Buku Lopatulika12 ndi omanga miyala ndi osema miyala, ndi kugula mitengo ndi miyala yosema kukakonza mogamuka nyumba ya Yehova, ndi zonse zoigulira nyumba zoikonzera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndi omanga miyala ndi osema miyala, ndi kugula mitengo ndi miyala yosema kukakonza mogamuka nyumba ya Yehova, ndi zonse zoigulira nyumba zoikonzera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ankalipiranso amisiri omanga ndi miyala ndi osema miyala, ndiponso ankagula mitengo ndi miyala yokumba yokonzera Nyumba ya Chauta, kudzanso zinthu zina zilizonse zofunikira poikonza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 amisiri a miyala ndiponso anthu ophwanya miyala. Iwo ankagula matabwa ndi miyala yosema yokonzera Nyumba ya Yehova ndipo ankalipira zinthu zonse zofunika pokonzanso nyumbayo. Onani mutuwo |