Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 12:11 - Buku Lopatulika

11 Napereka ndalama zoyesedwa m'manja mwa iwo akuchita ntchitoyi, akuyang'anira nyumba ya Yehova; ndipo iwo analipira nazo amisiri a mitengo ndi omanga, akugwira ntchito ya pa nyumba ya Yehova,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Napereka ndalama zoyesedwa m'manja mwa iwo akuchita ntchitoyi, akuyang'anira nyumba ya Yehova; ndipo iwo analipira nazo amisiri a mitengo ndi omanga, akugwira ntchito ya pa nyumba ya Yehova,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsono ndalamazo ataziyesa, ankazipereka kwa akapitao okonzetsa Nyumba ya Chauta aja. Iwowo ankalipira amisiri a matabwa ndi amisiri omanga nyumba, amene ankagwira ntchito yokonza Nyumba ya Chautayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ankati akadziwa kuti ndalamazo zilipo zingati, ankazipereka kwa anthu amene ankayangʼanira ntchito yokonza nyumbayo. Ndalamazo ankalipira anthu amene ankagwira ntchito yokonza Nyumba ya Yehova, amisiri a matabwa ndi amisiri omanga nyumba,

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 12:11
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Hiramu mfumu ya Tiro anatumiza mithenga kwa Davide ndi mitengo yamkungudza, ndi amisiri a matabwa, ndi omanga nyumba; iwo nammangira Davide nyumba.


Ndipo pakuona kuti ndalama zidachuluka m'bokosimo, anakwerako mlembi wa mfumu, ndi mkulu wa ansembe, nazimanga m'matumba, naziyesa ndalama zopereka m'nyumba ya Yehova.


ndi omanga miyala ndi osema miyala, ndi kugula mitengo ndi miyala yosema kukakonza mogamuka nyumba ya Yehova, ndi zonse zoigulira nyumba zoikonzera.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa