2 Mafumu 12:1 - Buku Lopatulika1 Chaka chachisanu ndi chiwiri cha Yehu, Yowasi analowa ufumu wake; nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mai wake ndiye Zibiya wa ku Beereseba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Chaka chachisanu ndi chiwiri cha Yehu, Yowasi analowa ufumu wake; nakhala mfumu m'Yerusalemu zaka makumi anai; ndi dzina la mai wake ndiye Zibiya wa ku Beereseba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chaka chachisanu ndi chiŵiri cha ufumu wa Yehu, Yowasi adaloŵa ufumu ndipo adalamulira zaka makumi anai ku Yerusalemu. Mai wake anali Zibiya wa ku Beereseba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Mʼchaka chachisanu ndi chiwiri cha Yehu, Yowasi anakhala mfumu, ndipo analamulira mu Yerusalemu zaka makumi anayi. Amayi ake anali Zibiya wa ku Beeriseba. Onani mutuwo |