2 Mafumu 11:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo magawo awiri a inu, ndiwo onse otulukira pa Sabata, azilindira nyumba ya Yehova kuzinga mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo magawo awiri a inu, ndiwo onse otulukira pa Sabata, azilindira nyumba ya Yehova kuzinga mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono enawo a m'zigawo ziŵiri zija odzaŵeruka ntchito pa Sabata, iwo adzalonde ku Nyumba ya Chauta, kuti aziteteza mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ndipo inu amene muli mʼmagulu ena awiri amene simugwira ntchito pa tsiku la Sabata, nonse mudzalondere mfumu ku nyumbayo. Onani mutuwo |