2 Mafumu 11:21 - Buku Lopatulika21 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa iye ufumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri polowa iye ufumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Yowasiyo anali wa zaka zisanu ndi ziŵiri pamene adaloŵa ufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yowasi anali wa zaka zisanu ndi ziwiri pamene anayamba kulamulira. Onani mutuwo |