2 Mafumu 11:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo otumikira anakhala chilili yense ndi zida zake m'manja mwake, kuyambira mbali ya kulamanja kufikira mbali ya kulamanzere ya nyumbayo, ku guwa la nsembe, ndi kunyumba, kuzinga mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo otumikira anakhala chilili yense ndi zida zake m'manja mwake, kuyambira mbali ya kulamanja kufikira mbali ya kulamanzere ya nyumbayo, ku guwa la nsembe, ndi kunyumba, kuzinga mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono adandanditsa asilikaliwo kuti aziteteza mfumu, aliyense ali ndi zida m'manja mwake, kuzungulira guwalo ndiponso Nyumbayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Alondawo, aliyense ali ndi chida mʼmanja mwake, anayima mozungulira mfumu, pafupi ndi guwa lansembe ndi nyumbayo, kuchokera mbali ya kummwera mpaka mbali ya kumpoto kwa nyumbayo. Onani mutuwo |