2 Mafumu 11:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo wansembeyo anapereka kwa atsogoleri a mazana mikondo ndi zikopa, zinali za mfumu Davide, zosungika m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo wansembeyo anapereka kwa atsogoleri a mazana mikondo ndi zikopa, zinali za mfumu Davide, zosungika m'nyumba ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Wansembeyo adapatsa atsogoleri aja mikondo ndi zishango, zimene zidaali za mfumu Davide. Zimenezi zinkasungidwa m'Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndipo wansembeyo anawapatsa asilikaliwo mikondo ndi zishango zimene zinali za mfumu Davide ndipo zinali mʼNyumba ya Yehova. Onani mutuwo |