2 Mafumu 11:1 - Buku Lopatulika1 Pamene Ataliya make wa Ahaziya anaona kuti mwana wake wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yachifumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamene Ataliya make wa Ahaziya anaona kuti mwana wake wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yachifumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ataliya, mai wake wa Ahaziya, ataona kuti mwana wake wafa, adanyamuka nakaononga onse a pa banja laufumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ataliya amayi ake a Ahaziya ataona kuti mwana wawo wafa, ananyamuka nakawononga banja lonse la mfumu. Onani mutuwo |