Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 10:36 - Buku Lopatulika

36 Ndipo masiku ake akukhala Yehu mfumu ya Israele mu Samariya ndiwo zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

36 Ndipo masiku ake akukhala Yehu mfumu ya Israele m'Samariya ndiwo zaka makumi awiri mphambu zisanu ndi zitatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

36 Yehu adalamulira Aisraele ku Samariya zaka 28.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

36 Yehu analamulira Aisraeli ku Samariya zaka 28.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 10:36
2 Mawu Ofanana  

Nagona Yehu ndi makolo ake, namuika mu Samariya. Ndi Yehowahazi mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Pamene Ataliya make wa Ahaziya anaona kuti mwana wake wafa, ananyamuka, naononga mbeu yonse yachifumu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa