2 Mafumu 10:26 - Buku Lopatulika26 Natulutsa zoimiritsa zija zinali m'nyumba ya Baala, nazitentha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Natulutsa zoimiritsa zija zinali m'nyumba ya Baala, nazitentha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndipo adatulutsamo chipilala chopatulika chimene chinali m'nyumba ya Baala nakachitentha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Iwo anakatulutsa mwala wopatulika umene unali mʼnyumba ya Baala ndipo anawutentha. Onani mutuwo |
Ndipo mfumu inalamulira Hilikiya mkulu wa ansembe, ndi ansembe a gawo lachiwiri, ndi olindira pakhomo, atulutse mu Kachisi wa Yehova zipangizo adazipangira Baala, ndi chifanizo adazipangira Baala, ndi chifanizo chija, ndi khamu lonse la kuthambo; nazitentha kunja kwa Yerusalemu ku thengo la ku Kidroni, natenga phulusa lake kunka nalo ku Betele.