2 Mafumu 10:22 - Buku Lopatulika22 Nati kwa iye wosunga nyumba ya zovala, Tulutsira otumikira Baala onse zovala. Nawatulutsira zovala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Nati kwa iye wosunga nyumba ya zovala, Tulutsira otumikira Baala onse zovala. Nawatulutsira zovala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono Yehu adauza munthu wosunga zovala kuti, “Bwera ndi zovala zopatulika zokwanira anthu onse opembedza Baala.” Munthuyo adaŵatengera zovalazo anthu aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndipo Yehu anawuza munthu wosunga mikanjo kuti, “Bweretsa mikanjo yokwanira atumiki onse a Baala.” Ndipo iye anabweretsa mikanjoyo. Onani mutuwo |