2 Mafumu 10:16 - Buku Lopatulika16 Nati iye, Tiye nane, ukaone changu changa cha kwa Yehova. M'mwemo anamuyendetsa m'galeta wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nati iye, Tiye nane, ukaone changu changa cha kwa Yehova. M'mwemo anamuyendetsa m'galeta wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndipo adamuuza kuti, “Tiye kuno, uwone m'mene ndikudziperekera kwa Chauta.” Motero adayenda naye m'galeta mwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yehu anati, “Tiye kuno uwone mmene ndikudziperekera kwa Yehova.” Ndipo anayenda naye mʼgaleta mwake. Onani mutuwo |