2 Mafumu 10:12 - Buku Lopatulika12 Pamenepo ananyamuka, nachoka, namuka ku Samariya. Ndipo pokhala kunyumba yosengera ya abusa panjira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Pamenepo ananyamuka, nachoka, namuka ku Samariya. Ndipo pokhala kunyumba yosengera ya abusa panjira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pambuyo pake Yehu adanyamuka napita ku Samariya. Atafika pa malo otchedwa “Pogona abusa,” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kenaka Yehu ananyamuka kupita ku Samariya. Atafika pa malo otchedwa Beti-Ekedi wa abusa, Onani mutuwo |