Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 1:18 - Buku Lopatulika

18 Machitidwe ake ena tsono adawachita Ahaziya, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Machitidwe ake ena tsono adawachita Ahaziya, sanalembedwa kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Tsono ntchito zina za Ahaziya pamodzi ndi zonse zimene adazichita zidalembedwa m'buku la Mbiri ya Mafumu a Aisraele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Ntchito zina zonse zimene Ahaziya anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Israeli?

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 1:18
15 Mawu Ofanana  

Ndipo machitidwe ena a Yerobowamu m'mene umo anachitira ufumu, taona, analembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele.


Tsono machitidwe ena a Ahabu, ndi zonse adazichita, ndi nyumba ya minyanga adaimanga, ndi mizinda yonse adaimanga, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Motero anafa monga mwa mau a Yehova adanena Eliyawo. Ndipo Yehoramu analowa ufumu m'malo mwake chaka chachiwiri cha Yehoramu mwana wa Yehosafati mfumu ya Yuda, pakuti analibe mwana wamwamuna.


Ndipo machitidwe ena a Yehu, ndi zonse anazichita, ndi mphambu yake yonse, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Machitidwe ena tsono a Yowasi, ndi zonse anazichita, ndi mphamvu yake yochita nkhondo nayo pa Amaziya mfumu ya Yuda, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Machitidwe ena tsono a Yehowahazi, ndi zonse anazichita, ndi mphamvu yake, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Machitidwe ena tsono a Yehowasi adazichita, ndi mphamvu yake, ndi umo analimbana naye Amaziya mfumu ya Yuda, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Machitidwe ena tsono a Yerobowamu, ndi zonse anazichita, ndi mphamvu yake, umo anachita nkhondo, nabweza kwa Israele Damasiko ndi Hamati amene anali a Yuda, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Machitidwe ena tsono a Zekariya, taonani, zalembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele.


Machitidwe ena tsono a Menahemu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Israele?


Nachita choipa pamaso pa Yehova, sanaleke zolakwa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele.


Machitidwe ena tsono a Pekahiya ndi zonse anazichita, taonani zalembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele.


Nachita choipa pamaso pa Yehova, osaleka zolakwa za Yerobowamu mwana wa Nebati, zimene analakwitsa nazo Israele.


Machitidwe ena tsono a Peka, ndi zonse anazichita, taonani, zalembedwa m'buku la machitidwe a mafumu a Israele.


Ndipo kunali, pamene Yehova adati akweze Eliya kumwamba ndi kamvulumvulu, Eliya anachokera ku Giligala pamodzi ndi Elisa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa