Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Akorinto 11:33 - Buku Lopatulika

33 ndipo mwa zenera, mudengu, ananditsitsa pakhoma, ndipo ndinapulumuka m'manja mwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 ndipo mwa zenera, mudengu, ananditsitsa pakhoma, ndipo ndinapulumuka m'manja mwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 Koma anthu adandiika m'dengu nanditsitsira pa windo la m'lingalo, motero ndidamthaŵira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 Koma abale anandiyika mʼdengu nanditsitsira pa chipupa kudzera pa zenera la mpandawo, motero ndinapulumuka mʼmanja mwake.

Onani mutuwo Koperani




2 Akorinto 11:33
4 Mawu Ofanana  

Moyo wathu unaonjoka ngati mbalame mu msampha wa msodzi; msampha unathyoka ndi ife tinaonjoka.


koma ophunzira ake anamtenga usiku, nampyoletsa palinga, namtsitsa mu dengu.


Taona, tikadzalowa m'dzikomo ife, uzimanga chingwe ichi chofiira pazenera pamene watitsitsira; ndipo udzasonkhanitsa m'nyumbamo atate wako ndi mai wako ndi abale ako ndi a m'nyumba onse a atate wako.


Chomwecho Mikala anamtsitsira Davide pazenera, namuka iye, nathawa, napulumuka.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa