2 Akorinto 11:28 - Buku Lopatulika28 Popanda zakunjazo pali chondisindikiza tsiku ndi tsiku, chalabadiro cha Mipingo yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Popanda zakunjazo pali chondisindikiza tsiku ndi tsiku, chalabadiro cha Mipingo yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Kuwonjezera pa zonsezi, tsiku ndi tsiku ndimapsinjidwa ndi udindo wa kusamalira mipingo yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Kuwonjezera pa zonsezi, tsiku ndi tsiku ndimakhala pa chipsinjo cha nkhawa ya mipingo yonse. Onani mutuwo |