1 Yohane 5:5 - Buku Lopatulika5 Koma ndani iye wogonjetsa dziko lapansi, koma iye amene akhulupirira kuti Yesu ndiye Mwana wa Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma ndani iye wogonjetsa dziko lapansi, koma iye amene akhulupirira kuti Yesu ndiye Mwana wa Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndani amagonjetsa dziko lapansi? Amaligonjetsa si wina ai, koma wokhulupirira kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndani amagonjetsa dziko lapansi? Yekhayo amene amakhulupirira kuti Yesu ndi Mwana wa Mulungu. Onani mutuwo |