1 Yohane 5:13 - Buku Lopatulika13 Izi ndakulemberani, kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha, inu amene mukhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Izi ndakulemberani, kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha, inu amene mukhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Inu amene mumakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu, ndakulemberani zimenezi kuti mudziŵe kuti muli ndi moyo wosatha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ine ndikulemba zimenezi kwa inu, amene mwakhulupirira dzina la Mwana wa Mulungu kuti mudziwe kuti muli ndi moyo wosatha. Onani mutuwo |