1 Yohane 5:12 - Buku Lopatulika12 Iye wakukhala ndi Mwana ali nao moyo; wosakhala ndi Mwana wa Mulungu alibe moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Iye wakukhala ndi Mwana ali nao moyo; wosakhala ndi Mwana wa Mulungu alibe moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Amene ali ndi Mwanayo, ali nawo moyo. Amene sali ndi Mwana wa Mulungu, alibe moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iye amene ali ndi Mwana ali ndi moyo, amene alibe Mwana wa Mulungu alibe moyo. Onani mutuwo |