1 Yohane 5:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo uwu ndi umboniwo, kuti Mulungu anatipatsa ife moyo wosatha, ndipo moyo umene uli mwa Mwana wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo uwu ndi umboniwo, kuti Mulungu anatipatsa ife moyo wosatha, ndipo moyo umene uli mwa Mwana wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Umboniwo tsono ndi wakuti Mulungu adatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowo umapezeka mwa Mwana wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndipo umboniwo ndi uwu: Mulungu anatipatsa moyo wosatha, ndipo moyowu uli mwa Mwana wake. Onani mutuwo |