1 Yohane 4:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo ife tapenyera, ndipo tichita umboni kuti Atate anatuma Mwana akhale Mpulumutsi wa dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo ife tapenyera, ndipo tichita umboni kuti Atate anatuma Mwana akhale Mpulumutsi wa dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Ife taona, ndipo tikuchita umboni, kuti Atate adatuma Mwana wake kuti adzakhale Mpulumutsi wa anthu a pa dziko lonse lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo taona ndipo tikuchitira umboni, kuti Atate anatuma Mwana wake kuti akhale Mpulumutsi wa dziko lapansi. Onani mutuwo |