1 Yohane 4:13 - Buku Lopatulika13 m'menemo tizindikira kuti tikhala mwa Iye, ndi Iye mwa ife, chifukwa anatipatsako Mzimu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 m'menemo tizindikira kuti tikhala mwa Iye, ndi Iye mwa ife, chifukwa anatipatsako Mzimu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Tikudziŵa kuti timakhala mwa Mulungu, ndipo Iyenso amakhala mwa ife, chifukwa adatipatsa Mzimu wake Woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ife tikudziwa kuti timakhala mwa Iye ndipo Iyeyo amakhala mwa ife chifukwa anatipatsa Mzimu wake. Onani mutuwo |