1 Yohane 4:11 - Buku Lopatulika11 Okondedwa, ngati Mulungu anatikonda ife kotero, ifenso tiyenera kukondana wina ndi mnzake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Okondedwa, ngati Mulungu anatikonda ife kotero, ifenso tiyenera kukondana wina ndi mnzake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Inu okondedwa, ngati Mulungu adatikonda kwambiri chotere, ifenso tiyenera kumakondana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Anzanga okondedwa, popeza Mulungu anatikonda chotere, ifenso tiyenera kukondana wina ndi mnzake. Onani mutuwo |