1 Yohane 3:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo lamulo lake ndi ili, kuti tikhulupirire dzina la Mwana wake Yesu Khristu, ndi kukondana wina ndi mnzake monga anatilamulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo lamulo lake ndi ili, kuti tikhulupirire dzina la Mwana wake Yesu Khristu, ndi kukondana wina ndi mnzake monga anatilamulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Chimene Mulungu amalamula nchakuti tizikhulupirira Mwana wake Yesu Khristu, ndipo kuti tizikondana monga Iye adatilamulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo lamulo lake ndi ili: kukhulupirira dzina la Mwana wake, Yesu Khristu, ndi kukondana wina ndi mnzake monga Iye anatilamulira. Onani mutuwo |