1 Yohane 3:21 - Buku Lopatulika21 Okondedwa, mtima wathu ukapanda kutitsutsa, tili nako kulimbika mtima mwa Mulungu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Okondedwa, mtima wathu ukapanda kutitsutsa, tili nako kulimbika mtima mwa Mulungu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Inu okondedwa, ngati mtima wathu sutitsutsa, titha kuima mopanda mantha pamaso pa Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Anzanga okondedwa, ngati mitima yathu sikutitsutsa, tili nako kulimbika mtima pamaso pa Mulungu. Onani mutuwo |