1 Yohane 3:18 - Buku Lopatulika18 Tiana, tisakonde ndi mau, kapena ndi lilime, komatu ndi kuchita ndi m'choonadi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Tiana, tisakonde ndi mau, kapena ndi lilime, komatu ndi kuchita ndi m'choonadi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ananu, chikondi chathu chisamangokhala cha nkhambakamwa chabe, koma chiziwoneka pa zochita zathu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Ana okondedwa, chikondi chathu chisakhale cha pakamwa pokha koma cha ntchito zathu ndi mʼchoonadi. Onani mutuwo |