1 Yohane 3:13 - Buku Lopatulika13 Musazizwe, abale, likadana nanu dziko lapansi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Musazizwe, abale, likadana nanu dziko lapansi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Motero musadabwe abale, anthu odalira zapansipano akamadana nanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Abale anga, musadabwe ngati dziko lapansi lidana nanu. Onani mutuwo |