1 Yohane 3:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti uwu ndi uthenga mudaumva kuyambira pachiyambi, kuti tikondane wina ndi mnzake: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti uwu ndi uthenga mudaumva kuyambira pachiyambi, kuti tikondane wina ndi mnzake: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Uthenga umene mudamva kuyambira pa chiyambi ndi wakuti tizikondana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Uthenga umene munawumva kuyambira pachiyambi ndi uwu: Tizikondana wina ndi mnzake. Onani mutuwo |