Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Yohane 2:26 - Buku Lopatulika

26 Izi ndakulemberani za iwo akusokeretsa inu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Izi ndakulemberani za iwo akusokeretsa inu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Ndikukulemberani zimenezi kuti ndikuuzeni za iwo aja amene amafuna kukusokeretsani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Ine ndikukulemberani zimenezi kuti ndikuwuzeni za amene akufuna kukusocheretsani.

Onani mutuwo Koperani




1 Yohane 2:26
12 Mawu Ofanana  

Wolungama atsogolera mnzake; koma njira ya oipa iwasokeretsa.


Popeza, inde popeza asokeretsa anthu anga, ndi kuti, Mtendere, pokhala palibe mtendere; ndipo anthu akamanga linga, aneneriwo alimata ndi dothi losapondeka;


pakuti adzauka Akhristu onyenga ndi aneneri onyenga, ndipo adzachita zizindikiro ndi zozizwitsa, kuti akasocheretse, ngati nkutheka, osankhidwa omwe.


Munthu aliyense asakunyengeni ndi kulanda mphotho yanu ndi kudzichepetsa mwini wake, ndi kugwadira kwa angelo, ndi kukhalira mu izi adaziona, wodzitukumula chabe ndi zolingalira za thupi lake, wosagwiritsa mutuwo,


Penyani kuti pasakhale wina wakulanda inu ngati chuma, mwa kukonda nzeru kwake, ndi chinyengo chopanda pake, potsata mwambo wa anthu, potsata zoyamba za dziko lapansi, osati potsata Khristu;


Koma Mzimu anena monenetsa, kuti m'masiku otsiriza ena adzataya chikhulupiriro, ndi kusamala mizimu yosocheretsa ndi maphunziro a ziwanda,


Koma anthu oipa ndi onyenga, adzaipa chiipire, kusokeretsa ndi kusokeretsedwa.


Tiana, munthu asasokeretse inu; iye wakuchita cholungama ali wolungama, monga Iyeyu ali wolungama:


Pakuti onyenga ambiri adatuluka kulowa m'dziko lapansi, ndiwo amene savomereza kuti Yesu Khristu anadza m'thupi. Ameneyo ndiye wonyenga ndi wokana Khristu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa