1 Yohane 2:23 - Buku Lopatulika23 Yense wakukana Mwana, alibe Atate; wovomereza Mwana ali ndi Atatenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Yense wakukana Mwana, alibe Atate; wovomereza Mwana ali ndi Atatenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Aliyense wokana Mwana, alibenso Atate. Wovomereza Mwana, alinso ndi Atate. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Aliyense wokana Mwana alibenso Atate. Wovomereza Mwana alinso ndi Atate. Onani mutuwo |