Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Yohane 2:23 - Buku Lopatulika

23 Yense wakukana Mwana, alibe Atate; wovomereza Mwana ali ndi Atatenso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Yense wakukana Mwana, alibe Atate; wovomereza Mwana ali ndi Atatenso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Aliyense wokana Mwana, alibenso Atate. Wovomereza Mwana, alinso ndi Atate.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Aliyense wokana Mwana alibenso Atate. Wovomereza Mwana alinso ndi Atate.

Onani mutuwo Koperani




1 Yohane 2:23
15 Mawu Ofanana  

Zinthu zonse zinaperekedwa kwa Ine ndi Atate wanga; ndipo palibe munthu adziwa Mwana, koma Atate yekha, ndi palibe wina adziwa Atate, koma Mwana yekha, ndi iye amene Mwana afuna kumuululira.


Zonse zaperekedwa kwa Ine ndi Atate wanga; ndipo palibe munthu azindikira Mwana ali yani, koma Atate; ndipo Atate ali yani, koma Mwana, ndi iye amene Mwana afuna kumuululira Iye.


Ine ndi Atate ndife amodzi.


Ndipo izi adzachita, chifukwa sanadziwe Atate, kapena Ine.


Koma moyo wosatha ndi uwu, kuti akadziwe Inu Mulungu woona yekha, ndi Yesu Khristu amene munamtuma.


kuti onse akalemekeze Mwana, monga alemekeza Atate. Wosalemekeza Mwana salemekeza Atate amene anamtuma Iye.


Chifukwa chake ananena ndi Iye, Ali kuti Atate wanu? Yesu anayankha, Simudziwa kapena Ine, kapena Atate wanga; mukadadziwa Ine, mukadadziwanso Atate wanga.


Wabodza ndani, koma iye wokanayo kuti Yesu siali Khristu? Iye ndiye wokana Khristu, amene akana Atate ndi Mwana.


Iye amene adzavomereza kuti Yesu ali Mwana wa Mulungu, Mulungu akhala mwa iye, ndi iye mwa Mulungu.


M'menemo muzindikira Mzimu wa Mulungu: mzimu uliwonse umene uvomereza kuti Yesu Khristu anadza m'thupi, uchokera mwa Mulungu;


Yense wokhulupirira kuti Yesu ndiye Khristu wabadwa kuchokera kwa Mulungu; ndipo yense wakukonda Iye amene anabala akondanso iye amene anabadwa wochokera mwa Iye.


Ndipo tidziwa kuti Mwana wa Mulungu wafika, natipatsa ife chidziwitso, kuti tizindikire Woonayo, ndipo tili mwa Woonayo, mwa Mwana wake Yesu Khristu. Iye ndiye Mulungu woona ndi moyo wosatha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa