1 Yohane 2:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo dziko lapansi lipita, ndi chilakolako chake; koma iye amene achita chifuniro cha Mulungu akhala kunthawi yonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo dziko lapansi lipita, ndi chilakolako chake; koma iye amene achita chifuniro cha Mulungu akhala kunthawi yonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Ndipotu dziko lapansi likupita, pamodzi ndi zake zonse zimene anthu amazilakalaka. Koma munthu wochita zimene Mulungu afuna, amakhalapo mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Dziko lapansi likupita pamodzi ndi zilakolako zake, koma amene amachita chifuniro cha Mulungu amakhalapo mpaka muyaya. Onani mutuwo |