1 Yohane 2:10 - Buku Lopatulika10 Iye amene akonda mbale wake akhala m'kuunika, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Iye amene akonda mbale wake akhala m'kuunika, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma munthu wokonda mnzake, amakhala m'kuŵala, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Aliyense amene amakonda mʼbale wake amakhalanso mʼkuwunika, ndipo mwa iye mulibe chokhumudwitsa. Onani mutuwo |