1 Yohane 1:10 - Buku Lopatulika10 Tikanena kuti sitidachimwe, timuyesa Iye wonama, ndipo mau ake sakhala mwa ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Tikanena kuti sitidachimwa, timuyesa Iye wonama, ndipo mau ake sakhala mwa ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tikanena kuti sitidachimwe, tikumuyesa wonama Mulungu, ndipo mau ake sali mwa ife. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ife tikanena kuti sitinachimwe, tikumutenga Mulungu kukhala wonama, ndipo Mawu ake sali mwa ife. Onani mutuwo |