Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 5:7 - Buku Lopatulika

7 Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda chilema.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda chilema.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Uziŵalamula zimenezi, kuti akhale opanda mlandu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Pereka malangizo amenewa kwa anthu kuti akhale opanda zolakwa.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 5:7
7 Mawu Ofanana  

kuti mukakhale osalakwa ndi oona, ana a Mulungu opanda chilema pakati pa mbadwo wokhotakhota ndi wopotoka, mwa iwo amene muonekera monga mauniko m'dziko lapansi,


Monga ndinakudandaulira iwe utsalire mu Efeso, popita ine ku Masedoniya, nditeronso, kuti ukalamulire ena ajawa asaphunzitse kanthu kena,


Lamulira izi, nuziphunzitse.


Lamulira iwo achuma m'nthawi ino ya pansi pano, kuti asadzikuze, kapena asayembekezere chuma chosadziwika kukhala kwake, koma Mulungu, amene atipatsa ife zonse kochulukira, kuti tikondwere nazo;


Ndikuchitira umboni pamaso pa Mulungu ndi Khristu Yesu, amene adzaweruza amoyo ndi akufa, ndi pa maonekedwe ake ndi ufumu wake;


Umboni uwu uli woona. Mwa ichi uwadzudzule mokalipa, kuti akakhale olama m'chikhulupiriro,


Izi lankhula, ndipo uchenjeze, nudzudzule ndi ulamuliro wonse. Munthu asakupeputse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa