1 Timoteyo 5:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda chilema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda chilema. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Uziŵalamula zimenezi, kuti akhale opanda mlandu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pereka malangizo amenewa kwa anthu kuti akhale opanda zolakwa. Onani mutuwo |