Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 5:12 - Buku Lopatulika

12 pokhala nacho chitsutso, popeza adataya chikhulupiriro chao choyamba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 pokhala nacho chitsutso, popeza adataya chikhulupiriro chao choyamba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Pamenepo amapezeka olakwa, chifukwa chosasunga lonjezo lao loyamba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Zikatero amadziweruza okha chifukwa aphwanya lonjezo lawo loyamba.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 5:12
8 Mawu Ofanana  

Israele wachitaya chokoma, mdani adzamlondola.


Ngati wina ali ndi njala adye kwao; kuti mungasonkhanire kwa chiweruziro. Koma zotsalazo ndidzafotokoza pakudza ine.


Ndizizwa kuti msanga motere mulikupatuka kwa iye amene anakuitanani m'chisomo cha Khristu, kutsata Uthenga Wabwino wina;


Koma amasiye aang'ono uwakane; pakuti pamene ayamba kumchitira Khristu chipongwe afuna kukwatiwa;


Ndipo aphunziraponso kuchita ulesi, aderuderu; koma osati ulesi wokha, komatunso alankhula zopanda pake, nachita mwina ndi mwina, olankhula zosayenera.


Musakhale aphunzitsi ambiri, abale anga, podziwa kuti tidzalangika koposa.


Chifukwa yafika nthawi kuti chiweruziro chiyambe pa nyumba ya Mulungu; koma ngati chiyamba ndi ife, chitsiriziro cha iwo osamvera Uthenga Wabwino wa Mulungu chidzakhala chiyani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa