1 Timoteyo 5:1 - Buku Lopatulika1 Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mkulu usamdzudzule, komatu umdandaulire ngati atate; anyamata ngati abale; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Munthu wachikulire usamdzudzule mokalipa, koma umchenjeze monga ngati bambo wako. Amuna achinyamata uzikhalitsana nawo ngati abale ako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Usadzudzule munthu wachikulire mokalipa, koma umuchenjeze ngati abambo ako. Achinyamata uwatenge ngati abale ako. Onani mutuwo |