Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




1 Timoteyo 4:9 - Buku Lopatulika

9 Okhulupirika mauwa ndi oyenera kulandiridwa konse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Okhulupirika mauwa ndi oyenera kulandiridwa konse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Ameneŵa ndi mau otsimikizika oyenera kuŵavomereza ndi mtima wonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Amenewa ndi mawu odalirika ndi oyenera kuwalandira kwathunthu.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 4:9
2 Mawu Ofanana  

Mbuye wake anati kwa iye, Chabwino, kapolo iwe wabwino ndi wokhulupirika; unali wokhulupirika pa zinthu zazing'ono, ndidzakhazika iwe pa zinthu zambiri; lowa iwe m'chikondwerero cha mbuye wako.


Mauwa ali okhulupirika ndi oyenera konse kuti awalandire, kuti Khristu Yesu anadza kudziko lapansi kupulumutsa ochimwa; wa iwowa ine ndine woposa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa