1 Timoteyo 4:7 - Buku Lopatulika7 koma nkhani zachabe ndi za akazi okalamba ukane. Ndipo udzizoloweretse kuchita chipembedzo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 koma nkhani zachabe ndi za akazi okalamba ukane. Ndipo udzizoloweretse kuchita chipembedzo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma upewe nthano zachabe, monga zimene akazi okalamba amakonda kukamba. Udzizoloŵeze kukhala ndi moyo wolemekeza Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma upewe nkhani zachabe ndi nthano za amayi okalamba; mʼmalo mwake udziphunzitse kukhala moyo wolemekeza Mulungu. Onani mutuwo |