1 Timoteyo 4:6 - Buku Lopatulika6 Ngati ukumbutsa abale zinthu izi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa m'mauwo a chikhulupiriro, ndi malangizo abwino amene udawatsata; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ngati ukumbutsa abale zinthu izi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa m'mauwo a chikhulupiriro, ndi malangizo abwino amene udawatsata; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ngati abale uŵalangiza zimenezi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa ndi mau a chikhulupiriro ndi a chiphunzitso choona chimene wakhala ukutsata. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ngati abale uwalangiza zimenezi, udzakhala mtumiki wabwino wa Khristu Yesu, woleredwa mʼchoonadi cha chikhulupiriro ndi mʼchiphunzitso chabwino chimene wakhala ukutsata. Onani mutuwo |