1 Timoteyo 4:13 - Buku Lopatulika13 Kufikira ndidza ine, usamalire kuwerenga, kuchenjeza, kulangiza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Kufikira ndidza ine, usamalire kuwerenga, kuchenjeza, kulangiza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Mpaka pamene ndidzabwere, uchite khama kuŵerengera anthu mau a Mulungu, kuŵalalikira ndi kuŵaphunzitsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Mpaka nditabwera, udzipereke powerenga mawu a Mulungu kwa anthu, kulalikira ndi kuphunzitsa. Onani mutuwo |