Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 4:11 - Buku Lopatulika

11 Lamulira izi, nuziphunzitse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Lamulira izi, nuziphunzitse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Uzilamula ndi kuphunzitsa zimenezi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Lamulira ndi kuphunzitsa zinthu zimenezi.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 4:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo izi ulamulire, kuti akhale opanda chilema.


Ndipo iwo akukhala nao ambuye okhulupirira, asawapeputse popeza ali abale; koma makamaka awatumikire popeza ali okhulupirira ndi okondedwa, oyanjana nao pa chokomacho. Izi uphunzitse, nuchenjeze.


lalikira mau; chita nao pa nthawi yake, popanda nthawi yake; tsutsa, dzudzula, chenjeza, ndi kuleza mtima konse ndi chiphunzitso.


Izi lankhula, ndipo uchenjeze, nudzudzule ndi ulamuliro wonse. Munthu asakupeputse.


Okhulupirika mauwa, ndipo za izi ndifuna kuti ulimbitse mau, kuti iwo akukhulupirira Mulungu asamalire akhalebe atsogoleri a ntchito zabwino. Izi nzokoma ndi zopindulitsa anthu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa