Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




1 Timoteyo 3:9 - Buku Lopatulika

9 okhala nacho chinsinsi cha chikhulupiriro m'chikumbu mtima choona.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 okhala nacho chinsinsi cha chikhulupiriro m'chikumbu mtima choona.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Akhale anthu a mtima wopanda kanthu koutsutsa posunga zoona za chikhulupiriro zimene Mulungu adaulula.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ayenera kugwiritsa mozama choonadi cha chikhulupiriro ndi kukhala ndi chikumbumtima chabwino.

Onani mutuwo Koperani




1 Timoteyo 3:9
4 Mawu Ofanana  

ndi kukhala nacho chikhulupiriro ndi chikumbumtima chokoma, chimene ena adachikankha, chikhulupiriro chao chidatayika;


koma chitsirizo cha chilamuliro ndicho chikondi chochokera mu mtima woyera ndi m'chikumbu mtima chokoma ndi chikhulupiriro chosanyenga;


Ndipo povomerezeka, chinsinsi cha kuchitira Mulungu ulemu nchachikulu: Iye amene anaonekera m'thupi, anayesedwa wolungama mumzimu, anapenyeka ndi angelo, analalikidwa mwa amitundu, wokhulupiridwa m'dziko lapansi, wolandiridwa mu ulemerero.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa