1 Timoteyo 3:8 - Buku Lopatulika8 Momwemonso atumiki akhale olemekezeka, osanena pawiri, osamwetsa vinyo, osati a chisiriro chonyansa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Momwemonso atumiki akhale olemekezeka, osanena pawiri, osamwetsa vinyo, osati a chisiriro chonyansa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Chimodzimodzinso ndi atumiki a mpingo: akhale ochita zachiukulu, osanena paŵiripaŵiri, osakhala ozoloŵera zoledzeretsa, osakonda udyo phindu la ndalama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Momwemonso atumiki, akhale anthu oyenera ulemu, woona mtima, osakhala okonda zoledzeretsa, osakonda kupeza zinthu mwachinyengo. Onani mutuwo |