1 Timoteyo 3:7 - Buku Lopatulika7 Kuyeneranso kuti iwo akunja adzakhoza kumchitira umboni wabwino; kuti ungamgwere mtonzo, ndi msampha wa mdierekezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Kuyeneranso kuti iwo akunja adzakhoza kumchitira umboni wabwino; kuti ungamgwere mtonzo, ndi msampha wa mdierekezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kuwonjezera pamenepo, akhale munthu woti ndi akunja omwe amamlemekeza, mwinamwina nkudzayamba kunyozedwa nagwa mu msampha wa Satana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ayeneranso kukhala munthu wambiri yabwino ndi akunja, kuti anthu asamutonze nagwa mu msampha wa Satana. Onani mutuwo |