1 Timoteyo 3:6 - Buku Lopatulika6 Asakhale wophunza, kuti podzitukumula ungamgwere mlandu wa mdierekezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Asakhale wophunza, kuti podzitukumula ungamgwere mlandu wa mdierekezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Asakhale munthu wolandiridwa mu mpingo chatsopano, kuwopa kuti angadzitukumule nkulangidwa monga momwe Satana adalangidwira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Asakhale wongotembenuka mtima kumene kuopa kuti angadzitukumule napezeka pa chilango monga Satana. Onani mutuwo |